Choonadi chodabwitsa ponena za mmene zimakhalira zovuta kukhala wabwino.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kodi nthawi zina mumamva ngati zonse zikukutsutsani? Umu ndi mmene ndikumvera lero
Mmene chiwopsezo cha bomba chinayesera chidaliro changa mwa Mulungu.
Ndaphunzira kuti njira yokhala ndi anthu ovuta ndi kuphunzira kusamalira zochita zanga.
M'pofunika kumvetsa kuti kuchimwa ndi kuyesedwa ku uchimo ndi zinthu ziwiri zosiyana.
Aliyense amafuna mtendere wadziko lonse, koma kupangamtendere kumayamba ndi ine
Werengani mmene achinyamata ena amachitira zimenezi pa moyo wawo wa tsiku ndi tsiku
Nchifukwa chiyani mumalankhula zoterezo? Kodi mukudandaula kuti ena aganiza zotani za inu? Kodi mukufuna kumasulidwa?
Tonse tikudziwa kuti kuimba mlandu ena sikumathandiza konse munyengo yotere, komabe mchitidwe wotere uli mu mkhalidwe wathu wokonda kuchita zoipa kuyambira pachiyambi …