Mndandanda wa zinthu zimene sindingathe kuchita ndi wosatha. Koma ndikhoza kuchita mbali yaing'ono yomwe ili patsogolo panga.
Kodi mungamve bwanji kudziwa kuti moyo wanu wakhala wopanda pake?
Pafupifupi Akristu onse amayang'ana chimene chiri chachikulu, ndipo amafuna kuti ana awo akhale aakulu m'dziko. Koma zimenezi si zimene Mulungu amafuna kwa ife!
Ndinadziŵa kuti sindinali kukhala ndi moyo monga wophunzira, kufikira pamene chokumana nacho chosintha moyo chinandikakamiza kuyandikira kwa Mulungu.
Yesu akutiuza kuti tiyenera kubadwanso. Kodi timachita bwanji zimenezi?
Ndawerenga Baibulo ndi kuphunzirapo kanthu pa moyo wanga wonse, koma kodi ndingadziwe bwanji motsimikiza kuti Baibulo ndi loonadi?
M'chipinda chathu chopempherera "chachinsinsi" timakhala ndi mgwirizano wapamtima ndi Mulungu, ndipo kumeneko tili ndi mphamvu yaikulu!
N'zovuta kwambiri kufotokoza zimene chikhulupiriro chili m'mawu ochepa chabe, koma pali zinthu zingapo zofunika zimene zingatithandize kumvetsa bwino.
Lonjezo lalikulu kwambiri limene Mulungu watipatsa n'lakuti tingasinthe kotheratu!
Sindinayembekezere kukhala munthu wokhulupirira Mulungu.
Chikhulupiriro chingasinthe zinthu, ngakhale usiku wamdima kwambiri. Kodi mumakhulupirira zimenezo?
Tonsefe tili ndi zinthu kapena anthu amene timatembenukira pamene tikufuna chitonthozo. Koma kodi mumapeza chitonthozo chenicheni ndi chokhalitsa?
Phunziro la kuimilira m'chikhulupiriro, kuchokera kwa mwana wamasiye amene anakhala mfumukazi.