Ndinadziŵa kuti sindinali kukhala ndi moyo monga wophunzira, kufikira pamene chokumana nacho chosintha moyo chinandikakamiza kuyandikira kwa Mulungu.
Kodi mungamve bwanji kudziwa kuti moyo wanu wakhala wopanda pake?
Mndandanda wa zinthu zimene sindingathe kuchita ndi wosatha. Koma ndikhoza kuchita mbali yaing'ono yomwe ili patsogolo panga.
Pafupifupi Akristu onse amayang'ana chimene chiri chachikulu, ndipo amafuna kuti ana awo akhale aakulu m'dziko. Koma zimenezi si zimene Mulungu amafuna kwa ife!
Awa ndi mavesi angapo onena za lonjezo laulemerero la Mulungu kwa ife: tingagonjetse uchimo!
Nkhondo ya Mayi wina pa kudziyerekeza ndi ena.
Pali kusiyana kwakukulu. Ndipo n'kofunika kwambiri kudziwa kusiyana kwake.
Kukhala Mkristu n'kwabwino kwambiri kuposa mmene tingaganizire.
Kodi ndikugwiritsa ntchito bwanji mwayi umenewu?
Machimo ambiri amagwirizana mwachindunji ndi mfundo zitatu zazikuluzi.
Ife tonse tili ndi zilakolako zoipa mu thupi lathu zimene zimatichititsa kuchita uchimo. Kodi tingapulumutsidwe bwanji ku vuto limeneli?
Baibulo limanena zokhala pamaso pa Mulungu osati pamaso pa anthu.Koma zimenezi zamatanthauza chiyani pa moyo wa tsiku ndi tsiku?
Mu mkhalidwe uliwonse, pali chinthu chimodzi chomwe mungathe kulamulira.