Kukhulupirira si kungovomereza kuti Baibulo ndi loona.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
M'Baibulo, Yesu wapatsidwa mayina osiyanasiyana. Kodi munayamba mwaganizapo za zimene ena mwa mayina ndi maudindo amenewa amatanthauza kwa ife patokha?