Choonadi chodabwitsa ponena za mmene zimakhalira zovuta kukhala wabwino.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Ndaphunzira kuti njira yokhala ndi anthu ovuta ndi kuphunzira kusamalira zochita zanga.
Ngakhale kuti Anelle wakhala akukhala ndi matenda kwa zaka zambiri, iye ndi mtsikana amene waphunzira kukhala wokhutira kwambiri.
Kodi zingatheke bwanji kuti tisamade nkhawa ndi chilichonse m’dziko limene zinthu zambiri n’zosatsimikizika?