Kodi mumakhulupiriradi ubwino ndi mphamvu za Mulungu? Kapena kodi mukuganiza kuti Mulungu ndi wofooka ngati inuyo?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Tonse tikudziwa kuti nthawi imene tili padziko lapansi ndi yochepa. Kodi tidzakhala titapindula chiyani panthaŵiyo?
Ndi mwa chikhulupiriro mwa Mulungu kuti tifika ku tsogolo limene Iye watikonzera.
Pali nkhondo yoti timenye, nkhondo yolimbana ndi uchimo, umene ulu muzu wa mazunzo onse.
Ndaona kuti Mulungu wathu ndi wamkulu kwambiri, komanso kuti m'Mawu a Mulungu muli machiritso ndi thandizo lalikulu bwanji.