Debora anali mneneri wamkazi ndi woweruza mu Israyeli. Iye ali chitsanzo champhamvu cha mmene chikhulupiriro m'zochita chimagwirira ntchito!
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Iye anali chabe mtsikana wabwinobwino wa ku Nazarete, koma anakhala mayi wa Yesu Kristu. Chifukwa chiyani iye?
Samueli anali wopatulika kuyambira umwana wake wonse. Moyo wake umatiwonetsa ubwino omvetsera mawu a Mulungu ndi kuwamvera ,nthawi zonse.