Ngakhale kuti nthawi zambiri malingaliro anga amaoneka kuti amasintha popanda chenjezo, ndaphunzira chinsinsi choti ndiwalamulire kuti asandilamulire.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Ndi mwa chikhulupiriro mwa Mulungu kuti tifika ku tsogolo limene Iye watikonzera.
Pamene ndilingalira za chiitano changa monga Mkristu, kodi ndili ndi chidwi chotani m'kuchikwaniritsa?
Kodi ndingasunge bwanji moyo wanga woganiza kukhala woyera pamene ambiri mwa malingaliro awa angobwera popanda ine kuwafuna?
M'pofunika kumvetsa kuti kuchimwa ndi kuyesedwa ku uchimo ndi zinthu ziwiri zosiyana.
Kodi tiyenera kugonjetsa chiyani? N'chifukwa chiyani zili zoipa kwambiri?
Nchifukwa chiyani mumalankhula zoterezo? Kodi mukudandaula kuti ena aganiza zotani za inu? Kodi mukufuna kumasulidwa?
Sitifunikira kudziimba mlandu pamene tikuyesedwa. Pano pali chifukwa chake ...