Ndi bwino kuti tidzifufuze kuti tione ngati Yesu adakali woyamba m'moyo wathu.
Ndinasangalala podziwa kuti Mulungu anandilenga mmene ndiliri.
Ndikamayenda m'kuunika, moyo umakhala wabwino, ndipo nthawi zonse ndimakhala ndi chikumbumtima chabwino. Koma kodi ndimayenda bwanji m'kuunika?
Kodi munayamba mwaganizapo kapena kunena mawu amenewa? Kodi mukudziwa zimene Mulungu anauza Yeremiya pamene ananena zimenezi?
Tingaphunzire zambiri pa nkhani ya Yosefe.
Kodi munthu aliyense angasankhe bwanji kuti moyo wina wa munthu ndi wopanda mtengo kuposa wawo?
Kodi kupambana kwa Davide pa Goliati kungakhale chitsanzo chotani kwa ife masiku ano?
Ngati mukufuna kutsimikizira munthu wina kuti akhale Mkhristu, moyo wokhulupirika umalankhula mokweza kuposa mawu
Nthaŵi yathu pano padziko lapansi yokhala ndi chibadwa chaumunthu chochimwa, ingakhale ngati kuyenda m'munda wa mabomba. Kodi timadutsa bwanji bwinobwino?
Kuti mupeze mtendere wa Mulungu umene udzasunga mtima ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu, muyenera kumenyana!
N'zotheka kuika chikhulupiriro changa chonse mwa Mulungu. Amatsogolera moyo wanga.
Aliyense amafuna mtendere wadziko lonse, koma kupangamtendere kumayamba ndi ine
M'pofunika kumvetsa kuti kuchimwa ndi kuyesedwa ku uchimo ndi zinthu ziwiri zosiyana.
Nchifukwa chiyani mumalankhula zoterezo? Kodi mukudandaula kuti ena aganiza zotani za inu? Kodi mukufuna kumasulidwa?
Chidani ndi mawu amphamvu. Kodi tiyenera kudanadi ndi atate ndi amayi athu, mkazi ndi ana, abale ndi alongo, ndipo ngakhale ife eni?