Kuti mupeze mtendere wa Mulungu umene udzasunga mtima ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu, muyenera kumenyana!
Aliyense amafuna mtendere wadziko lonse, koma kupangamtendere kumayamba ndi ine
N'zotheka kuika chikhulupiriro changa chonse mwa Mulungu. Amatsogolera moyo wanga.
Nchifukwa chiyani mumalankhula zoterezo? Kodi mukudandaula kuti ena aganiza zotani za inu? Kodi mukufuna kumasulidwa?
M'pofunika kumvetsa kuti kuchimwa ndi kuyesedwa ku uchimo ndi zinthu ziwiri zosiyana.
Chidani ndi mawu amphamvu. Kodi tiyenera kudanadi ndi atate ndi amayi athu, mkazi ndi ana, abale ndi alongo, ndipo ngakhale ife eni?