Kodi "chigololo" n'chiyani mogwirizana ndi Mawu a Mulungu ndipo zotsatira za chigololo n'zotani?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kodi lingaliro lodetsedwa pang'ono nlowopsa motani?
Kodi ndimachita chiyani ndi maganizo amene sakondweretsa Mulungu?
Kodi mukufuna kuthana bwanji ndi zilakolako zanu zauchimo? Kodi ndinu wofunitsitsa kuthawa machimo awa mpaka mutapeza zomwe mukufunadi – ndiko kugonjetsa iwo?
"Ndinalidi ndi kulakalaka kukhala womasuka ku malingaliro odetsedwa koma njira yochitira zimenezi sinali yomveka bwino."
Chiyero ndi chinthu chomwe chikukhala chachilendo kwambiri.
Timawerenga zambiri zokhudza mtima wa m'Baibulo. Koma kodi mtima wathu kwenikweni nchiyani, kunena mwauzimu? Kodi mtima wathu uli ndi kufunika kotani?
Zochitika zake zatsimikizira kuti moyo uno ndi weniweni.
Pamene ndilingalira za chiitano changa monga Mkristu, kodi ndili ndi chidwi chotani m'kuchikwaniritsa?
Kodi ndingasunge bwanji moyo wanga woganiza kukhala woyera pamene ambiri mwa malingaliro awa angobwera popanda ine kuwafuna?
Mothandizidwa ndi uthenga wabwino n'zotheka kukhala wopanda zolaula kwathunthu.