Tikudziwa kuti Baibulo limanena kuti Mulungu amatikonda. Koma kodi Iye ali kuti m'nthaŵi zovuta?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Ndi bwino kuti tidzifufuze kuti tione ngati Yesu adakali woyamba m'moyo wathu.
Kodi Yesu angatilamule bwanji kuti tizikonda anthu? Kodi mungatani kuti muzikonda munthu wina?
Kuona anthu monga mmene Mulungu amawaonera, kumatithandiza pamene tili ndi zochita ndi anthu amphamvu, olamulira.
Kodi tikudziwa bwanji kuti Mulungu amatikonda? Chofunika kwambiri: Kodi Mulungu amadziwa bwanji kuti timamukonda?
Kodi chochititsa chenicheni cha kusagwirizana konse ndi mikangano nchiyani?
Kodi munayamba mwakayikirapo kuti Mulungu amakukondani? Mavesi a m'Baibulo amenewa angasinthe zimenezo.
Nkhani ya Mariya ndi Elizabeti m'Baibulo imafotokoza za ubwenzi wabwino kwambiri. Kodi n'chiyani chinapangitsa ubwenzi wawo kukhala wolimba kwambiri?
Kodi zolinga ndi zotsatira za chikondi changa n'zotani? Kodi ndili ndi chikondi chomwe chimangoganizira za ine ndekha kapena chikondi chopatsa moyo, chopanda dyera?