Lamulo la Mulungu ndi losavuta komanso lomveka bwino: "Uskakhala ndi mulungu wina aliyense koma ine." Eksodo 20:3
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kukayikira koipa n'kosiyana kotheratu ndi chitsanzo chosiyidwa ndi Kristu, ndipo kumachokera ku kusoŵeka kwa chikondi. Koma pali njira yotulukira m'malingaliro oipa ameneŵa!
Kodi mukuchita chinachake mwachangu kuti musiye kuchimwa?
Chilichonse chimene timanena chimachokera ku malingaliro athu.
Kodi ndingasunge bwanji moyo wanga woganiza kukhala woyera pamene ambiri mwa malingaliro awa angobwera popanda ine kuwafuna?
Njira ya moyo wanga imapangidwa ndi zosankha za tsiku ndi tsiku zomwe ndimapanga.
"Maganizo anu ndi aulere," iwo akutero. Koma kodi zilidi? Kodi mumakhala ndi ufulu weniweni m'moyo wanu woganiza?