Zochitika zake zatsimikizira kuti moyo uno ndi weniweni.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Pamene ndilingalira za chiitano changa monga Mkristu, kodi ndili ndi chidwi chotani m'kuchikwaniritsa?
Kodi ndingasunge bwanji moyo wanga woganiza kukhala woyera pamene ambiri mwa malingaliro awa angobwera popanda ine kuwafuna?