Zochitika zake zatsimikizira kuti moyo uno ndi weniweni.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Mmene timaganizira ndi kuchitira ndi anthu osoŵa, osauka ndi amene dziko limawayang'ana pansi, zimasonyeza zimene timaganiza ponena za Mulungu, Mlengi.
Kodi mwamvapo za njira ya "tsopano"?
Ndinali nditazolowera kuvomereza mabodza ake, mpaka Mulungu anandisonyeza zimene zinafunika kusintha pa moyo wanga.
Sukulu zina zimakhala ndi masiku "owonetsera ndi kuuza". Ndinaganiza za momwe zimenezo zimagwiriranso ntchito pamene tikufuna kugawana uthenga wabwino ndi ena ..
Yesu ankatha kuona mmene Natanayeli analili asanalankhule ndi Iye. Kodi n'chiyani chinali chapadera kwambiri pa Natanayeli?
Cholinga cha Satana ndicho kutilekanitsa ndi Mulungu. Umu ndi mmene tingamuletsere.
Cholinga sichiri kukhala ndi zambiri monga momwe zingathere za dziko lino, koma kuleka zonse.
Pangakhale zifukwa zambiri za "kuchita chinthu choyenera". Kodi chifukwa chanu n'chiyani?
Pali chiweruzo chomwe chiri chothandizira, ndipo pali chiweruzo chomwe chiri choipa ndi chovulaza. Chimodzi ndi kuwala ndipo chimodzi ndi mdima. Werengani zambiri apa!
Pali kusiyana kwakukulu pakati pa anthu odzitcha Akhristu. Ndi angati tinganene kuti akulemekezadi Mulungu ndi moyo umene akukhala?