"Kodi tsogolo lanu likuoneka bwanji? Kodi mwakonza moyo wanu?" Ndinayenera kuima ndi kuganiza ndisanayankhe.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kugonekedwa m'chipatala ndi COVID-19, mavesi a m'Baibulo omwe adapitiriza kubwera m'maganizo mwake anali chinachake choti Hermen agwire.
"Kodi aliyense wa inu mwa kuda nkhawa kuwonjezera ola limodzi pa moyo wanu??" —Mateyu 6:27
Pangakhale zifukwa zambiri zimene timayesedwera kuda nkhaŵa, koma tili ndi mphamvu yaikulu koposa m'chilengedwe chonse kumbali yathu!
Kuona anthu monga mmene Mulungu amawaonera, kumatithandiza pamene tili ndi zochita ndi anthu amphamvu, olamulira.
Ndinasangalala podziwa kuti Mulungu anandilenga mmene ndiliri.
Kuti mupeze mtendere wa Mulungu umene udzasunga mtima ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu, muyenera kumenyana!
N'zotheka kuika chikhulupiriro changa chonse mwa Mulungu. Amatsogolera moyo wanga.
Mmene chiwopsezo cha bomba chinayesera chidaliro changa mwa Mulungu.
Ukada nkhawa, umamupangitsa Mulungu kukhala wamng’ono komanso kuti iweyo ukhale wamkulu. Kunena zoona mukunena kuti Mulungu ndi wabodza.