"Kodi ndimapita kuti kuchokera pano?" linali funso lomwe linali kuyaka mumtima mwa mnyamata wina wa ku Cameroon atatembenuzidwa.
"Ngakhale mutakhala kuti kapena muli ndani, mukhoza kukhala wosangalala kwambiri."
Fedora akufotokoza mmene anakhalira womasuka kotheratu ku mkwiyo wake woipa.