Pokhala ndi "chidziwitso" chochuluka chomwe chilipo ndipo aliyense akuyesera kutiuza kuti akunena zoona, kodi n'zotheka bwanji kudziwa zomwe zilidi zoona?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Pamene ndilingalira za chiitano changa monga Mkristu, kodi ndili ndi chidwi chotani m'kuchikwaniritsa?