Mukhoza kuchotsa Satana ndi mabodza ake ndi chinyengo m'moyo wanu kamodzi kotheratu!
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Satana akamagwira ntchito pakati pa anthu a Mulungu, amagwiritsa ntchito zilakolako zawo zachibadwa ndi zinthu zimene zimawakopa.
Mmene mungagonjetsere mabodza ndi zinenezo za Satana.
Kumveka kwina pa nkhani yosangalatsa yomwe nthawi zambiri imamvedwa molakwika.
Ndinali nditazolowera kuvomereza mabodza ake, mpaka Mulungu anandisonyeza zimene zinafunika kusintha pa moyo wanga.
Cholinga cha Satana ndicho kutilekanitsa ndi Mulungu. Umu ndi mmene tingamuletsere.