Ndife anthu. Timachimwa. Kodi ndi mapeto a nkhaniyi?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kodi ndimakhala ndi moyo kwa ndani? Kodi ndikutumikira Mulungu kapena anthu?
Pa Khirisimasi timaganiza za Mpulumutsi wathu. Koma kodi zimenezo zikutanthauzanji kwa ife?
Kodi muli ndi Mkulu wa Ansembe amene amamvetsetsa zofooka zanu ndi kukuthandizani kugonjetsa?
M'Baibulo, Yesu wapatsidwa mayina osiyanasiyana. Kodi munayamba mwaganizapo za zimene ena mwa mayina ndi maudindo amenewa amatanthauza kwa ife patokha?
Kodi mwaganizapo za Yesu, Mwana yekhayo wa Mulungu, ndi zimene Iye anachita kuti tikhale abale ndi alongo ake?
Chidani ndi mawu amphamvu. Kodi tiyenera kudanadi ndi atate ndi amayi athu, mkazi ndi ana, abale ndi alongo, ndipo ngakhale ife eni?