Kunyada ndi tchimo limene limakhudza munthu aliyense.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Julia ataona kuti anali wonyada komanso wodzikuza, ankadziwa kuti pali chinachake chimene angachite.
Kukhala ngati Mwana wa Mulungu kumadalira chinthu chimodzi chofunika kwambiri chimenechi.
Timanyadira kwambiri zomwe sitikuziwona n'komwe. Koma Mulungu akufuna kutimasula ku zimenezo!
Vesi ili lili ngati mgwirizano pakati pa ine ndi Mulungu: "Mulungu amatsutsana ndi onyada, koma Iye amapereka chisomo kwa odzichepetsa.".
Kodi ndingatsimikizire bwanji kuti ndikugwiritsa ntchito luso langa kwa Mulungu?