Kodi ndimakhulupirira kuti moyo wachikristu monga momwe wafotokozedwera m'Baibulo ndi wotheka? N'zosavuta kukhumudwa.
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Ndinkalimbana kwambiri ndi maganizo amdima komanso kukhumudwa. Pano pali momwe zonse zinasinthira.
Ndinali nditazolowera kuvomereza mabodza ake, mpaka Mulungu anandisonyeza zimene zinafunika kusintha pa moyo wanga.