N'zosavuta kutumiza mauthenga kudzera pa Intaneti. Koma kodi mwaganizapo za zotsatira zake?
Kodi ndili ndi ufulu wotumikira Mulungu, kapena ndimamangidwa ndi zimene ena angaganize ponena za ine?
Werengani nkhani yosonkhezera imeneyi yonena za kukhulupirika kwenikweni kwa Danieli, ndi chikhulupiriro chake mwa Mulungu zivute zitani.
N'chifukwa chiyani nthawi zonse mumakhala woyamikira komanso wosangalala, mosasamala kanthu za mmene zinthu zilili pa moyo wanu kapena mmene mukumvera.
Pali njira imodzi yokha yodziŵiradi Yesu.
Kodi ndimakhala ndi moyo kwa ndani? Kodi ndikutumikira Mulungu kapena anthu?
Iye anali chabe mtsikana wabwinobwino wa ku Nazarete, koma anakhala mayi wa Yesu Kristu. Chifukwa chiyani iye?