Pokhala ndi "chidziwitso" chochuluka chomwe chilipo ndipo aliyense akuyesera kutiuza kuti akunena zoona, kodi n'zotheka bwanji kudziwa zomwe zilidi zoona?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kodi munayamba mwakayikirapo kuti Mulungu amakukondani? Mavesi a m'Baibulo amenewa angasinthe zimenezo.
Kukhulupirira si kungovomereza kuti Baibulo ndi loona.
M'Baibulo, Yesu wapatsidwa mayina osiyanasiyana. Kodi munayamba mwaganizapo za zimene ena mwa mayina ndi maudindo amenewa amatanthauza kwa ife patokha?