Mwina imeneyi ndi imodzi mwa mavesi odziwika bwino a m'Baibulo okhudzana ndi Pentekoste, koma kodi cholinga cha mphamvu imeneyi n'chiyani?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Kodi mwakumana ndi mphamvu yodabwitsa yomwe imabwera mukadzazidwa ndi Mzimu?
Kodi ndingayende bwanji mwa Mzimu?
Popeza sindingathe kugonjetsa uchimo popanda thandizo la Mzimu Woyera, n'kofunika kwambiri kuti ndimvetsere ndi kumvera pamene Mzimu akulankhula nane.
Kodi Mzimu Woyera ndani? N'chifukwa chiyani ndimamufuna?