Kukayika ndi chikhulupiriro: Zinthu zosiyana kwambiri zokhala ndi zotsatira zosiyana kwambiri! Kodi musankha chiyani?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Chikhulupiriro chingasinthe zinthu, ngakhale usiku wamdima kwambiri. Kodi mumakhulupirira zimenezo?
Yesu akutiuza kuti sitiyenera kuvutika ndi zinthu zoopsa zimene zimachitika m'dzikoli.
Pamene chiyembekezo chathu chili mwa Kristu, tili ndi chiyembekezo cha mtsogolo mu ulemerero waukulu ndi wosatha.
Tiyeni tiyambe chaka chatsopano chodzaza ndi chiyembekezo ndi chikhulupiriro chamoyo m'mawu onse a Mulungu.
Kodi mukugwira mwamphamvu chiyembekezo chimene mwaulula?
M'nkhondo ya tsiku ndi tsiku imene Mkristu ayenera kulimbana ndi uchimo, tiyenera kudziŵa mmene tingapitirizebe kuima!Zomwe zili mnkhaniyi;
Chimwemwe chachikulu chimenechi chimene angelo analankhula kalekale chinasintha zonse, ndipo chingasinthebe miyoyo yathu lero lino.
Tiyeni tiuze uthenga wabwino mosangalala za zonse zimene tsopano n'zotheka mwa chikhulupiriro mwa Yesu Kristu!