Kodi mumamva kukhala wosakhazikika ndipo kodi moyo wanu umawoneka wopanda pake? Kodi mumada nkhawa ndi zinthu zambiri ndipo kodi muli ndi mafunso ambiri?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Tsopano mwakonzeka kuyamba moyo watsopano wonse!
Kodi munayamba mwaganizapo kapena kunena mawu amenewa? Kodi mukudziwa zimene Mulungu anauza Yeremiya pamene ananena zimenezi?
Pamene Yesu anaukitsidwa kwa akufa ndipo Mzimu Woyera anabwera, anapereka chiyembekezo kwa ophunzira Ake onse – kuphatikizapo inu ndi ine! Werengani zambiri!
Pali kusiyana kwakukulu pakati pa anthu odzitcha Akhristu. Ndi angati tinganene kuti akulemekezadi Mulungu ndi moyo umene akukhala?
Kodi mwawerengera mtengo wake?