Kodi kupachikidwa ndi nsembe za Yesu zinali zosiyana bwanji ndi nsembe ndi chikhululukiro m'Pangano Lakale?
Moyo wa Chikirisitu Wochitachita
Yesu ndi Khristu, Mwana wa Mulungu Wamoyo, ndipo pa thanthwe ili ndi pamene Mpingo umamangidwa.
Ngati Kristu anabweradi m'thupi, m'chibadwa cha munthu, kodi chinali chibadwa chotani? N'chifukwa chiyani zimenezi zili zofunika?
Kodi mukudziwa kuti pa chilichonse chimene timachita, anthu adzaona moyo wa Khristu kapena moyo wa Satana mwa ife?
Ndife anthu. Timachimwa. Kodi ndi mapeto a nkhaniyi?