Kugonjetsa uchimo

“Kugonjetsa uchimo” zikutanthauza kuti simuchita tchimo lachodziwadziwa – chimene mukudziwa kuti ndi tchimo pa nthawi imene muyesedwa. Izi sizikutanthauza kuti mulibe uchimo, koma yesero limagonjetsedwa lisanakhale tchimo. ( Aroma 8:37; 1 Akorinto 15:57; Chivumbulutso 2:7 )